Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 34:14-17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

14. Akadzikumbukila yekha mumtima mwace,Akadzisonkhanitsira yekha mzimu wace ndi mpweya wace,

15. Zamoyo zonse zidzatsirizika pamodzi,Ndi munthu adzabwerera kupfumbi.

16. Ngati tsono uli nako kuzindikira, tamvera ici,Cherera khutu kunena kwanga.

17. Kodi munthu woipidwa naco ciweruzo adzalamulira?Ndipo kodi utsutsa wolungama ndi wamphamvuyo kuti ngwoipa?

Werengani mutu wathunthu Yobu 34