Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 34:1-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo Elihu anabwereza kunena, nati,

2. Tamverani mau anga, inu anzeru;Mundicherere khutu inu akudziwa.

3. Pakuti khutu liyesa mau,Monga m'kamwa mulawa cakudya.

4. Tidzisankhire coyeneraco,Tidziwe mwa tokha cokomaco.

5. Pakuti Yobu wanena, Ine ndine wolungama,Ndipo Mulungu wandicotsera coyenera ine.

6. Kodi ndidzinamizire?Bala langa nlosapola, ngakhale sindinalakwa.

Werengani mutu wathunthu Yobu 34