6. Taonani, ndikhala kwa Mulungu ngati inu;Inenso ndinaumbidwa ndi dothi,
7. Taonani, kuopsa kwanga simudzacita nako mantha;Ndi ici ndikusenzetsani sicidzakulemererani.
8. Zedi mwanena m'makutu mwanga,Ndinamvanso mau akunena kwanu, akuti,
9. Ndine woyera ine, wopanda kulakwa,Ndine wosaparamula, ndiribe mphulupulu.