Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 33:6-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Taonani, ndikhala kwa Mulungu ngati inu;Inenso ndinaumbidwa ndi dothi,

7. Taonani, kuopsa kwanga simudzacita nako mantha;Ndi ici ndikusenzetsani sicidzakulemererani.

8. Zedi mwanena m'makutu mwanga,Ndinamvanso mau akunena kwanu, akuti,

9. Ndine woyera ine, wopanda kulakwa,Ndine wosaparamula, ndiribe mphulupulu.

Werengani mutu wathunthu Yobu 33