Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 33:2-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

2. Taonani tsono, ndatsegula pakamwa panga,Lilime langa lanena m'kamwa mwanga.

3. Maneno anga aulula ciongoko ca mtima wanga,Ndi monga umo idziwira milomo yanga idzanena zoona.

4. Mzimu wa Mulungu unandilenga,Ndi mpweya wa Wamphamvuyonse umandipatsa moyo.

5. Ngati mukhoza, mundiyankhe;Mulongosolere mau anu pamaso panga, mukonzeke.

6. Taonani, ndikhala kwa Mulungu ngati inu;Inenso ndinaumbidwa ndi dothi,

Werengani mutu wathunthu Yobu 33