Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 32:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Elihu mwana wa Barakeli wa ku Buzi anayankha, nati,Ine ndine mnyamata, inu ndinu okalamba;Cifukwa cace ndinadziletsa, ndi kuopa kukuonetsani monga umo ndayesera ine.

Werengani mutu wathunthu Yobu 32

Onani Yobu 32:6 nkhani