18. Pakuti ndadzazidwa ndi mau,Ndi mzimu wa m'kati mwanga undifulumiza.
19. Taonani, m'cifuwa mwanga muli ngati vinyo wosowa popungulira,Ngati matumba atsopano akuti aphulike.
20. Ndidzanena kuti cifundo citsike;Ndidzatsegula milomo yanga ndi kuyankha.
21. Ndisati ndisamalire nkhope ya munthu,Kapena kumchula munthu maina omdyola nao;
22. Pakuti sindidziwa kuchula maina osyasyalika;Ndikatero Mlengi wanga adzandicotsa msanga.