Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 31:3-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Si ndizo cionongeko ca wosalungama,Ndi tsoka la ocita mphulupulu?

4. Nanga sapenyanjira zanga,Ndi kuwerenga moponda mwanga monse?

5. Ngati ndinayanjana nalo bodza,Ndi phazi langa linathamangira cinyengo;

6. Andiyese ndi muyeso wolingana,Kuti Mulungu adziwe ungwiro wanga.

7. Ngati phazi langa linapambuka m'njira,Ndi mtima wanga unatsata maso anga?Ngati cirema camamatira manja anga?

8. Ndibzale ine nadye wina,Ndi zondimerera ine zizulidwe.

Werengani mutu wathunthu Yobu 31