Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 30:10-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. Anyansidwa nane, akhala patali ndi ine,Saleka kuthira malobvu pankhope panga.

11. Pakuti anamasula nsinga zao, nandizunza;Anataya comangira m'kamwa mwao pamaso panga.

12. Ku dzanja langa lamanja anauka oluluka,Akankha mapazi anga,Andiundira njira zao zakundiononga.

13. Aipsa njira yanga,Athandizana ndi tsoka langa;Ndiwo anthu omwewo osowa mthandizi.

Werengani mutu wathunthu Yobu 30