Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 29:18-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

18. Pamenepo ndinati, Ndidzatsirizika m'cisa canga;Ndipo ndidzacurukitsa masiku anga ngati mcenga.

19. Muzu wanga watambalala kufikira kumadzi;Ndi mame adzakhala pa nthambi yanga usiku wonse.

20. Ulemu wanga udzakhala wosaguga mwa ine,Ndi uta wanga udzakhala wosalifuka m'dzanja mwanga.

21. Anthu anandimvera, nalindira,Nakhala cete, kuti ndiwapangire.

Werengani mutu wathunthu Yobu 29