Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 28:3-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Munthu athawitsa mdima,Nafunafuna mpaka malekezero onse,Miyala ya mdima wa bii ndi ya mthunzi wa imfa.

4. Aboola mgodi posiyana patali pokhala anthu;Aiwalika ndi phazi lopitapo;Apacikika kutali ndi anthu, nalendewa-lendewa.

5. Kunena za nthaka, kucokera momwemo mumaturuka cakudya,Ndi m'munsi mwace musandulizika ngati ndi moto.

Werengani mutu wathunthu Yobu 28