25. Pamene anaikira mphepo muyeso wace,Nayesera madzi miyeso;
26. Pakucitira mvula lamulo,Ndi njira yoyendamo mphezi ya bingu;
27. Pamenepo anaiona nzeru, naifotokozera;Anaikonza, naisanthula.
28. Koma kwa munthu anati,Taonani, kuopa Ambuye ndiko nzeru;Ndi kupatukana naco coipa ndiko luntha.