20. Koma nzeru ifuma kuti?Ndi luntha, pokhala pace pali kuti?
21. Popeza pabisikira maso a zamoyo zonse,Pabisikiranso mbalame za m'mlengalenga,
22. Cionongeko ndi Imfa zikuti,Tamva mbiri yace m'makutu mwathu.
23. Mulungu ndiye: azindikira njira yace,Ndiye adziwa pokhala pace.