Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 27:7-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Mdani wanga akhale ngati woipa,Ndi iye amene andiukira ngati wosalungama.

8. Pakuti ciyembekezo ca wonyoza Mulungu nciani pomlikhatu Mulungu,Pomcotsera moyo wace?

9. Kodi Mulungu adzamvera kupfuula kwace, ikamdzera nsautso?

10. Kodi adzadzikondweretsa naze Wamphamvuyonse,Ndi kuitana kwa Mulungu nthawi zonse?

11. Ndidzakulangizani za dzanja la Mulungu;Cokhala ndi Wamphamvuyonse sindidzacibisa.

Werengani mutu wathunthu Yobu 27