4. Potero munthu akhala bwanji wolungama kwa Mulungu?Kapena wobadwa ndi mkazi akhala woyera bwanji?
5. Taonani, ngakhale mwezi ulibe kuwala;Ndi nyenyezi siziyera pamaso pace;
6. Kopambana kotani nanga munthu, ndiye mphutsi!Ndi wobadwa ndi munthu, ndiyo nyongolotsi!