3. Ngati awerengedwa makamu ace?Ndipo ndaniyo, kuunika kwace sikumturukira?
4. Potero munthu akhala bwanji wolungama kwa Mulungu?Kapena wobadwa ndi mkazi akhala woyera bwanji?
5. Taonani, ngakhale mwezi ulibe kuwala;Ndi nyenyezi siziyera pamaso pace;