6. Pakuti wamtenga cikole kwa mbale wako wopanda cifukwa,Ndi kubvula ausiwa zobvala zao.
7. Sunampatsa wolema madzi amwe,Ndi wanjala unammana cakudya.
8. Koma munthu mwini mphamvu, dziko ndi lace;Ndi munthu wobvomerezeka, anakhala momwemo.
9. Unabweza akazi amasiye osawaninkha kanthu,Ndi manja a ana amasiye anatyoledwa.