25. Ndipo Wamphamvuyonse adzakhala cuma cako,Ndi ndarama zako zofunika.
26. Pakuti pamenepo udzakondwera naye Wamphamvuyonse,Ndi kuweramutsa nkhope yako kwa Mulungu.
27. Udzampemphera ndipo adzakumvera;Nudzatsiriza zowinda zako.
28. Ukatsimikiza mtima kakuti, kadzakhazikikira iwe;Ndi kuunika kudzawala pa njira zako.