Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 22:25-28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

25. Ndipo Wamphamvuyonse adzakhala cuma cako,Ndi ndarama zako zofunika.

26. Pakuti pamenepo udzakondwera naye Wamphamvuyonse,Ndi kuweramutsa nkhope yako kwa Mulungu.

27. Udzampemphera ndipo adzakumvera;Nudzatsiriza zowinda zako.

28. Ukatsimikiza mtima kakuti, kadzakhazikikira iwe;Ndi kuunika kudzawala pa njira zako.

Werengani mutu wathunthu Yobu 22