Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 2:7-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Naturuka Satana pamaso pa Yehova, nazunza Yobu ndi zironda zowawa, kuyambira ku phazi lace kufikira pakati pamutu pace.

8. Ndipo anadzitengera phale, kudzikanda nalo; nakhala pansi m'mapulusa.

9. Pamenepo mkazi wace ananena naye, Kodi uumiriranso kukhala wangwiro? citira Mulungu mwano, ufe.

Werengani mutu wathunthu Yobu 2