Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 2:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anati kwa Satana, Kodi waonerera mtumiki wanga Yobu? pakuti palibe wina wonga iye m'dzikomo, munthu wangwiro ndi woongoka, wakuopa Mulungu, ndi kupewa zoipa; naumirirabe kukhala wangwiro, cinkana undisonkhezera ndimuononge kopanda cifukwa.

Werengani mutu wathunthu Yobu 2

Onani Yobu 2:3 nkhani