Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 16:18-22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

18. Dziko iwe, usakwirire mwazi wanga,Ndi kulira kwanga kusowe popumira.

19. Tsopanonso, taona, mboni yanga iri kumwamba,Ndi nkhoswe yanga ikhala m'mwamba.

20. Mabwenzi anga andinyoza; Koma diso langa lilirira misozi kwa Mulungu;

21. Ha! munthu akadapembedzera mnzace kwa Mulungu,Monga munthu apembedzera mnansi wace!

22. Pakuti zitafika zaka zowerengeka,Ndidzamuka ku njira imene sindibwererako.

Werengani mutu wathunthu Yobu 16