Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yobu 13:21-25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

21. Mundicotsere dzanja lanu kutali,Ndi kuopsa kwanu kusandicititse mantha.

22. Pamenepo muitane, ndipo ndidzayankha;Kapena ndinene ndine, ndipo mundiyankhe ndinu.

23. Mphulupulu zanga ndi zocimwa zanga ndi zingati?Mundidziwitse kulakwa kwanga ndi cimo langa,

24. Mubisiranji nkhope yanu,Ndi kundiyesa mdani wanu?

25. Kodi mudzaopsa tsamba lakungouluka,Ndi kulondola ziputu zouma?

Werengani mutu wathunthu Yobu 13