18. Ndipo udzalimbika mtima popeza pali ciyembekezo;Nudzafunafuna, ndi kugona mosatekeseka,
19. Inde udzagona pansi, wopanda wina wakukunjenjemeretsa,Ndipo ambiri adzakupembedza,
20. Koma maso a oipa adzagoma, Ndi pothawirapo padzawasowa,Ndipo ciyembekezo cao ndico kupereka mzimu wao.