Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 9:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Manase adzadya Efraimu ndi Efraimu adzadya Manase, ndipo iwo pamodzi adzadyana ndi Yuda. Mwa izi zonse mkwiyo wace sunacoke, koma dzanja lace liri citambasulire.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 9

Onani Yesaya 9:21 nkhani