Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 8:16-19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Manga umboni, mata cizindikilo pacilamulo mwa aphunzi anga.

17. Ndipo ndidzalindira Yehova, amene wabisira a nyumba ya Yakobo nkhope yace, ndipo ndidzamyembekeza Iye,

18. Taonani, ine ndi ana amene Yehova wandipatsa ine, tiri zizindikilo ndi zodabwitsa mwa Israyeli, kucokera kwa Yehova wa makamu, amene akhala m'phiri la Ziyoni.

19. Ndipo pamene iwo adzati kwa iwe, Funa kwa olaula, ndi obwebweta, amene alira pyepye, nang'ung'udza; kodi anthu sadzafuna kwa Mulungu wao? Cifukwa ca amoyo, kodi adzafuna kwa akufa?

Werengani mutu wathunthu Yesaya 8