Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 65:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Atero Yehova, Monga vinyo watsopano apezedwa m'tsango, ndipo wina ati, Usaliononge, pakuti muli mdalitso m'menemo, momwemo ndidzacita cifukwa ca atumiki anga, kuti ndisawaononge onse.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 65

Onani Yesaya 65:8 nkhani