Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 65:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Sipadzakhalanso khanda la masiku, pena munthu wokalamba osakwanitsa masiku ace; pakuti mwana adzafa wa zaka zana limodzi; ndipo wocimwa pokhala wa zaka zana limodzi adzatembereredwa.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 65

Onani Yesaya 65:20 nkhani