Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 63:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndidzachula za cifundo cace ca Yehova, ndi matamando a Yehova, monga mwa zonse zimene Yehova wapereka kwa ife; ndi ubwino wace waukuru kwa banja la Israyeli, umene Iye wapereka kwa iwo, monga mwa cifundo cace, ndi monga mwa nchito zocuruka za cikondi cace.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 63

Onani Yesaya 63:7 nkhani