Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 6:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Caka cimene mfumu Uziya anafa, ndinaona Ambuye atakhala pa mpando wacifumu wautari, ndi wotukulidwa, ndi zobvala zace zinadzala m'Kacisi.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 6

Onani Yesaya 6:1 nkhani