Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 53:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace ndidzamgawira gawo ndi akuru; ndipo adzagawana ndi amphamvu zofunkha; pakuti Iye anathira moyo wace kuimfa; ndipo anawerengedwa pamodzi ndi olakwa; koma ananyamula macimo a ambiri, napembedzera olakwa.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 53

Onani Yesaya 53:12 nkhani