Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 51:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

atero Ambuye ako Yehova, ndi Mulungu wako amene anena mlandu wa anthu ace, Taona, ndacotsa m'dzanja mwako cikho conjenjemeretsa, ngakhale mbale ya cikho ca ukali wanga; iwe sudzamwa ico kawirinso.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 51

Onani Yesaya 51:22 nkhani