Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 5:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace monga ngati lilime la moto likutha ciputu, ndi monga udzu wouma ugwa pansi m'malawi, momwemo muzu wao udzakhala monga wobvunda, maluwa ao adzauluka m'mwamba ngati pfumbi; cifukwa kuti iwo akana cilamulo ca Yehova wa makamu, nanyoza mau a Woyera wa Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 5

Onani Yesaya 5:24 nkhani