Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 49:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yimbani inu, m'mwamba, nukondwere iwe dziko lapansi, yimbani inu mapiri, pakuti Yehova watonthoza mtima wa anthu ace, nadzacitira cifundo obvutidwa ace.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 49

Onani Yesaya 49:13 nkhani