Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 48:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Inde, iwe sunamva; inde, sunadziwe; inde, kuyambira kale khutu lako silinatsegudwe; pakuti ndinadziwa kuti iwe wacita mwaciwembu ndithu, ndipo unayesedwa wolakwa cibadwire.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 48

Onani Yesaya 48:8 nkhani