Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 48:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Imvani inu ici, banja la Yakobo, amene muchedwa ndi dzina la Israyeli, amene munaturuka m'madzi a Yuda amene mulumbira dzina la Yehova ndi kuchula dzina la Mulungu wa Israyeli, koma si m'zoona, pena m'cilungamo.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 48

Onani Yesaya 48:1 nkhani