Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 47:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace tsono, imva ici, iwe wotsata zokondweretsa, amene umakhala mosatekeseka, amene umati mumtima mwako, Ine ndine, ndipo popanda ine palibenso wina; sindidzakhala monga mkazi wamasiye, kapena kudziwa kumwalira kwa ana;

Werengani mutu wathunthu Yesaya 47

Onani Yesaya 47:8 nkhani