Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 46:8-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

8. Kumbukirani ici, nimucirimike, mudzikumbutsenso, olakwa inu.

9. Kumbukirani zinthu zoyamba zakale, kuti Ine ndine Mulungu, ndipo palibenso wina; Ine ndine Yehova, ndipo palibenso wina wofana ndi Ine;

10. ndilalikira za cimariziro kuyambira paciyambi, ndi kuyambira nthawi zakale ndinena zinthu zimene zisanacitidwe; ndi kunena, Uphungu wanga udzakhala, ndipo ndidzacita zofuna zanga zonse;

Werengani mutu wathunthu Yesaya 46