Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 42:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ine ndine Yehova; dzina langa ndi lomweli; ndipo ulemerero wanga Ine sindidzapereka kwa wina, ngakhale kunditamanda kwa mafano osemedwa.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 42

Onani Yesaya 42:8 nkhani