Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 41:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Chulani zinthu zimene zirinkudza m'tsogolo, kuti ife tidziwe kuti inu ndinu milungu; inde, citani zabwino, kapena citani zoipa, kuti ife tiopsyedwe, ndi kuona pamodzi.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 41

Onani Yesaya 41:23 nkhani