Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 39:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Hezekiya anakondwera nao, nawaonetsa nyumba yace ya cuma, siliva, ndi golidi, ndi zonunkhira, ndi mafuta okometsetsa, ndi nyumba yonse ya zida zace, ndi zonse zopezedwa m'zosungira zace; munalibe kanthu m'nyumba mwace, kapena m'dziko lace lonse, kamene Hezekiya sanawaonetsa.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 39

Onani Yesaya 39:2 nkhani