Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 37:36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mthenga wa Yehova anaturuka, naphaipha m'zitando za Asuri, zikwi zana ndi makumi asanu ndi atatu ndi zisanu, ndipo pamene anthu anauka mamawa, taonani, onse ndiwo mitembo.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 37

Onani Yesaya 37:36 nkhani