Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 37:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mukati kwa Hezekiya, mfumu ya Yuda, Asakunyenge Mulungu wako, amene iwe umkhulupirira, ndi kuti, Yerusalemu sadzaperekedwa m'manja mwa mfumu ya Asuri.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 37

Onani Yesaya 37:10 nkhani