Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 30:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Komanso kuwala kwace kwa mwezi kudzakhala ngati kuwala kwa dzuwa, ndi kuwala kwa dzuwa kudzakula monga madzuwa asanu ndi awiri, monga kuwala kwa masiku asanu ndi awiri, tsiku limenelo Yehova adzamanga bala la anthu ace, nadzapoletsa khana limene anawakantha ena.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 30

Onani Yesaya 30:26 nkhani