Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 29:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

cifukwa cace, taonani, ndidzacitanso mwa anthu awa nchito yodabwitsa, ngakhale nchito yodabwitsa ndi yozizwitsa; ndipo nzeru ya anthu ao anzeru idzatha, ndi luntha la anthu ao ozindikira lidzabisika.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 29

Onani Yesaya 29:14 nkhani