Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 28:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti Yehova adzauka monga m'phiri la Perazimu, nadzakwiya monga m'cigwa ca Gibeoni; kuti agwire nchito yace, nchito yace yacilendo, ndi kuti acite cocita cace, cocita cace cacilendo.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 28

Onani Yesaya 28:21 nkhani