Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 26:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ife tinali ndi pakati, ife tinamva zopweteka, tafanana ngati tabala mphepo; sitinacite cipulumutso ciri conse pa dziko lapansi; ngakhale okhala m'dziko lapansi sanagwe.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 26

Onani Yesaya 26:18 nkhani