Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 26:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Tsiku limenelo adzayimba nyimbo imeneyi m'dziko la Yuda, Ife tiri ndi mudzi wolimba; Iye adzaikacipulumutso cikhale macemba ndi malinga.

2. Tsegulani pazipata, kuti mtundu wolungama, umene ucita zoonadi, ulowemo.

3. Inu mudzasunga mtima wokhazikika mu mtendere weni weni, cifukwa ukukhulupirirani Inu.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 26