Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 22:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndidzaika mfungulo wa nyumba ya Davide paphewa pace, ndipo iye adzatsegula, ndipo palibe wina adzatseka, iye adzatseka ndipo palibe wina adzatsegula.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 22

Onani Yesaya 22:22 nkhani