Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 2:18-20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

18. Ndimo mafano adzapita psiti.

19. Anthu adzalowa m'mapanga a m'matanthwe, ndi m'maenje apansi, kuthawa kuopsya kwa Yehova, ndi ulemerero wacifumu wace, podzuka Iye kugwedeza dziko ndi mphamvu.

20. Tsiku limenelo munthu adzataya ku mfuko ndi ku mileme mafano ace asiliva ndi agolidi amene anthu anampangira iye awapembedze;

Werengani mutu wathunthu Yesaya 2