Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 14:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma iwe watayidwa kunja kwa manda ako, ngati nthambi yonyansa, ngati cobvala ca ophedwa, opyozedwa ndi lupanga, otsikira ku miyala ya dzenje, monga ngati mtembo wopondedwa ndi phazi.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 14

Onani Yesaya 14:19 nkhani