Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 13:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma zirombo za m'cipululu zidzagona pamenepo; nyumba zao zidzadzala ndi zakukuwa; ndipo nthiwatiwa zidzakhala pamenepo, ndipo atonde adzajidimuka pamenepo,

Werengani mutu wathunthu Yesaya 13

Onani Yesaya 13:21 nkhani